Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Kwa zaka zambiri Nsanja ya Olonda inalingaliridwa kukhala magazini a Akristu odzozedwa okha. Komabe, kuyambira mu 1935, chigogomezero chowonjezereka chinaperekedwa pa kulimbikitsa a “khamu lalikulu,” amene chiyembekezo chawo ndicho moyo wosatha padziko lapansi, kutenga ndi kuŵerenga Nsanja ya Olonda. (Chivumbulutso 7:9) Patapita zaka zingapo, mu 1940, Nsanja ya Olonda inali kugaŵiridwa nthaŵi zonse kwa anthu m’makwalala. Zaka zingapo pambuyo pake, chiŵerengero cha makope ofalitsidwa chinawonjezereka mofulumira.

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena