Mawu a M'munsi
d Mosangalatsa, liwu Lachigiriki kaamba ka kulira momveka (klaiʹo) lagwiritsidwa ntchito kwa Yesu pa chochitika pamene ananeneratu za kudza kwa chiwonongeko cha Yerusalemu. Cholembera cha Luka chikuti: “Ndipo mmene anayandikira, anaona mudziwo [Yerusalemu] naulirira.”—Luka 19:41.