Mawu a M'munsi
a Popeza Mikaeli ali m’ngelo wamkulu, ena amadzimva kuti kumuzindikiritsa iye monga Yesu kumachotsa m’njira ina yake ulemu kapena thayo la Yesu. (Yuda 9) Komabe, chitsimikizo kaamba ka chizindikiritso chimenecho chinatsogoza ophunzira otchulidwa pamwambapo Achipembedzo Chadziko kuzindikira Mikaeli monga Yesu mosasamala kanthu za chenicheni chakuti iwo mwinamwake amakhulupirira mu Utatu.