Mawu a M'munsi
a Levitiko 27:1-7 imalozera ku kuwomboledwa kwa aliyense payekha ‘kopatsidwa’ (mwa chowinda) ku kachisi monga wogwira ntchito. Mtengo wa chiwombolo unasiyanasiyana molingana ndi msinkhu. Pa msinkhu wa 60 mtengo umenewo unatsika kotheratu mwachiwonekere chifukwa munthu wa msinkhu umenewo analingaliridwa kukhala wosakhoza kugwira ntchito monga wachichepere. The Encyclopcedia Judaica mowonjezera ikunena kuti: “Malinga ndi Talmud, ukalamba . . . umayamba pa 60.”