Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w22 August tsamba 32
  • Nkhani Zimene Zatuluka Pa JW Library Komanso JW.ORG

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zatuluka Pa JW Library Komanso JW.ORG
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
w22 August tsamba 32

Nkhani Zimene Zatuluka Pa JW Library Komanso JW.ORG

ZOCHITIKA PA MOYO WA A MBONI ZA YEHOVA

Tinasankha Kukhala Moyo Wosalira Zambiri

Madián ndi Marcela anaona kuti kumangokhalira kugula zinthu komanso kukhala ndi ngongole zazikulu kunkachititsa kuti azikhala ndi nkhawa, koma kuphunzitsa anthu za Mulungu kunawathandiza kuti azisangalala.

NKHANI ZINA

Kodi Baibulo Lingakuthandizeni Pakachitika Ngozi Zam’chilengedwe?

Malangizo a m’Baibulo angakuthandizeni pasanachitike ngozi zam’chilengedwe, pamene zikuchitika komanso pambuyo pake.

MFUNDO ZOTHANDIZA MABANJA

Zimene Makolo Ayenera Kudziwa Zokhudza Kutumiza Mwana Kumalo Osamalira Ana Masana

Makolo asanasankhe kutumiza mwana wawo kumalo osamalira ana, ayenera kuganizira ubwino ndi kuipa kwake. Mafunso amene ali munkhaniyi angawathandize kudziwa zimene zingakhale zothandiza kwa mwana wawo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena