Magazini Yophunzira
JULY 2021
NKHANI ZOPHUNZIRA KUYAMBIRA: AUGUST 30–SEPTEMBER 26, 2021
© 2021 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
Magaziniyi sitigulitsa. Timaipereka ngati njira imodzi yophunzitsira anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo. Ngati mukufuna kupereka pitani pa donate.jw.org.
Malemba onse m’magaziniyi akuchokera mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika lolembedwa m’Chichewa chamakono, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina.
CHITHUNZI CHAPACHIKUTO:
Ophunzira a Yesu ankamukonda chifukwa sankadziona kukhala wapamwamba kuposa ena. Iye ankasangalala kucheza ndi anzake (Onani nkhani yophunzira 29, ndime 12)