Nkhani Zimene Zatuluka Pa JW Library Komanso JW.ORG
ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA
Kodi Ndingaphunzitse Bwanji Chikumbumtima Changa?
Chikumbumtima chanu chimasonyeza kuti ndinu munthu wotani. Chimasonyezanso mfundo zimene mumakhulupirira. Ndiye kodi chikumbumtima chanu chimasonyeza zotani zokhudza inuyo?
Pa JW Library, pitani pamene alemba kuti PUBLICATIONS > ARTICLE SERIES > YOUNG PEOPLE ASK.
Pa jw.org, pitani pamene alemba kuti LAIBULALE > NKHANI ZOSIYANASIYANA > ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA
TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO
Mariya Mmagadala yemwe anali ndi chikhulupiriro cholimba, anali wophunzira woyamba kumuona Yesu ataukitsidwa. Iye anapatsidwa mwayi woti auze ena uthenga wabwinowu.
Pa JW Library, pitani pamene alemba kuti PUBLICATIONS > ARTICLE SERIES > IMITATE THEIR FAITH.
Pa jw.org, pitani pamene alemba kuti LAIBULALE > NKHANI ZOSIYANASIYANA > TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO.