February 13-19
1 MBIRI 13-16
Nyimbo Na. 123 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (1 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Zinthu Zimatiyendera Bwino Tikamatsatira Malangizo”: (10 min.)
Mfundo Zothandiza: (10 min.)
1Mb 16:31—N’chifukwa chiyani Alevi anaimba kuti: “Yehova wakhala mfumu!”? (w14 1/15 10 ¶14)
Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?
Kuwerenga Baibulo: (4 min.) 1Mb 13:1-14 (th phunziro 11)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 18)
Ulendo Wobwereza: (4 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Mugawireni chimodzi mwa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 7)
Nkhani: (5 min.) w16.01 13-14 ¶7-10—Mutu: Kodi Tingasonyeze Bwanji Kuti Timayamikira Chikondi Cha Khristu?—2Ak 5:14. (th phunziro 8)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Khalani Bwenzi la Yehova—Muzimvetsera Tikakhala Pamisonkhano: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako ngati n’zotheka funsani ana omwe munawasankhiratu mafunso awa: N’chifukwa chiyani tiyenera kumamvetsera tikakhala pamisonkhano? Kodi n’chiyani chingakuthandizeni kuchita zimenezi?
Zofunika Pampingo: (10 min.)
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 37 mfundo 6 komanso zomwe taphunzira, kubwereza ndi zolinga
Mawu Omaliza (3 min.)
Nyimbo Na. 21 ndi Pemphero