December 27, 2021–January 2, 2022
OWERUZA 13-14
Nyimbo Na. 134 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (1 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Kodi Makolo Angaphunzire Chiyani kwa Manowa ndi Mkazi Wake?”: (10 min.)
Mfundo Zothandiza: (10 min.)
Owe 14:2, 3—Kodi mkazi wa Chifilisitiyu anali “woyenera” bwanji kwa Samisoni? (w05 3/15 26 ¶1)
Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?
Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Owe 14:5-20 (th phunziro 5)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
“Zimene Mungachite Kuti Muzisangalala Kwambiri mu Utumiki—Muzithandiza Ophunzira Anu Kuti Azidzidyetsa Mwauzimu”: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Muzithandiza Amene Mukuphunzira Nawo Baibulo Kuti Azidzidyetsa Mwauzimu.
Phunziro la Baibulo: (5 min.) lffi phunziro 02 zomwe taphunzira, kubwereza, komanso zolinga (th phunziro 17)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Zofunika Pampingo: (15 min.)
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lvs mutu 9 ndime 22-26, mfundo za m’Baibulo tsa. 129-131
Mawu Omaliza (3 min.)
Nyimbo Na. 35 ndi Pemphero