Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 September tsamba 10
  • October 11-17

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • October 11-17
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 September tsamba 10

October 11-17

YOSWA 10-11

  • Nyimbo Na. 149 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yehova Anamenyera Nkhondo Aisiraeli”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Yos 10:13​—N’chifukwa chiyani n’zosafunika kuti tidziwe zomwe zinali “m’buku la Yasari”? (w09 3/15 32 ¶5)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Yos 10:1-15 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • “Zimene Mungachite Kuti Muzisangalala Kwambiri mu Utumiki​—Muzilola Kuti Atumiki Anzanu Azikuthandizani”: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Muzigwiritsa Ntchito Zomwe Yehova Watipatsa Kuti Muzisangalala ndi Ntchito Yophunzitsa​—Abale Athu.

  • Phunziro la Baibulo: (5 min.) lffi phunziro 01 mfundo 4 (th phunziro 14)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 102

  • Zofunika Pampingo: (15 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lvs mutu 6 ndime 1-11

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 8 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena