Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 July tsamba 5
  • “Musamade Nkhawa”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Musamade Nkhawa”
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Posachedwapa, Sikudzakhalanso Mmphaŵi!
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Dziko Lopanda Umphawi Layandikira
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Limbikitsani Osauka
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
  • Mapeto a Umphaŵi Ayandikira
    Galamukani!—1998
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 July tsamba 5
Banja lomwe limapeza zinthu movutika likuyenda m’dera losauka kukakumana ndi abale ena kuti akachite zinthu zauzimu.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

“Musamade Nkhawa”

M’nthawi ya Aisiraeli Yehova ankathandiza anthu osauka. Kodi masiku ano iye amathandiza bwanji atumiki ake omwe ndi osauka?

  • Amawaphunzitsa kuti azikhala ndi maganizo oyenera pa nkhani ya ndalama.​—Lu 12:15; 1Ti 6:​6-8

  • Wawathandiza kuti azidziona moyenera. ​—Yob 34:19

  • Wawaphunzitsa kuti azigwira ntchito mwakhama komanso kupewa zizolowezi zoipa.​—Miy 14:23; 20:1; 2Ak 7:1

  • Wawabweretsa m’banja la Akhristu omwe amasonyezana chikondi.​—Yoh 13:35; 1Yo 3:​17, 18

  • Wawapatsa chiyembekezo.​—Sl 9:18; Yes 65:​21-23

Sitiyenera kuda nkhawa ngakhale tikumane ndi mavuto otani. (Yes 30:15) Tikapitiriza kufunafuna Ufumu choyamba, Yehova adzatithandiza kupeza zinthu zofunika pa moyo.​—Mt 6:​31-33.

ONERANI VIDIYO YAKUTI CHIKONDI CHANU CHISATHE NGAKHALE KUTI . . . MUKUVUTIKA NDI UMPHAWI​—CONGO, NDIPO KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Chithunzi cha muvidiyo yakuti ‘Chikondi Chanu Chisathe Ngakhale Kuti . . . Mukuvutika ndi Umphawi​—Congo.’ Gulu la abale ndi alongo likupita kumalo a msonkhano. Ambiri anyamula mipando komanso zinthu zina.

    Kodi abale omwe amakhala pafupi ndi malo a msonkhano anasonyeza bwanji chikondi polandira abale ndi alongo amene anachokera m’madera akutali?

  • Chithunzi cha muvidiyo yakuti ‘Chikondi Chanu Chisathe Ngakhale Kuti . . . Mukuvutika ndi Umphawi​—Congo.’ M’bale akuyala pabedi kunyumba kwake pokonzekera abale amene akuchokera kutali.

    Kodi vidiyoyi yatiphunzitsa chiyani zokhudza chikondi cha Yehova kwa anthu osauka?

  • Chithunzi cha muvidiyo yakuti ‘Chikondi Chanu Chisathe Ngakhale Kuti . . . Mukuvutika ndi Umphawi​—Congo.’ Abale akuvala pokonzekera msonkhano.

    Kodi tingatsanzire bwanji Yehova ngakhale titakhala ndi zinthu zochepa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena