JULY 12-18
DEUTERONOMO 13-15
Nyimbo Na. 38 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (1 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Kodi Chilamulo Chinkasonyeza Bwanji Kuti Yehova Amaganizira Anthu Osauka?”: (10 min.)
Mfundo Zothandiza: (10 min.)
De 14:21—Kodi tingaphunzire chiyani pa lamulo loletsa kuwiritsa mwana wa mbuzi mu mkaka wa mayi ake? (w06 4/1 31)
Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?
Kuwerenga Baibulo: (4 min.) De 13:1-18 (th phunziro 5)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Wobwereza: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Ulendo Wobwereza: Kuvutika—1Yo 5:19. Muziimitsa vidiyoyi nthawi iliyonse imene pali chizindikiro chosonyeza kuti muime n’kufunsa omvera mafunso omwe ali muvidiyoyi.
Ulendo Wobwereza: (3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza. (th phunziro 6)
Ulendo Wobwereza: (5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Mugawireni chimodzi mwa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 11)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
“Musamade Nkhawa”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Chikondi Chanu Chisathe Ngakhale Kuti . . . Mukuvutika ndi Umphawi—Congo.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lvs mutu 1 ndime 13-18, Mfundo za M’Baibulo tsa. 13-15, Mawu Akumapeto 4
Mawu Omaliza (3 min.)
Nyimbo Na. 37 ndi Pemphero