Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 October tsamba 2
  • October 1-7

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • October 1-7
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 October tsamba 2

October 1-7

YOHANE 9-10

  • Nyimbo Na. 25 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yesu Amasamalira Nkhosa Zake”: (10 min.)

    • Yoh. 10:1-3, 11, 14​—Yesu yemwe ndi “m’busa wabwino,” amadziwa nkhosa zake ndipo amazisamalira bwino kwambiri (“Khola la nkhosa” zithunzi ndi mavidiyo pa Yoh. 10:1, nwtsty; w11 5/15 7-8 ¶5)

    • Yoh. 10:4, 5​—Nkhosa zimadziwa mawu a Yesu osati mawu a alendo (cf 125 ¶17)

    • Yoh. 10:16​—Nkhosa za Yesu zimakhala zogwirizana (“kuzibweretsa” mfundo zimene ndikuphunzira pa Yoh. 10:16, nwtsty)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yoh. 9:38​—Kodi zimene munthu yemwe poyamba anali wakhungu anachita pogwadira Yesu zinkatanthauza chiyani? (“anamugwadira” mfundo zimene ndikuphunzira pa Yoh. 9:38, nwtsty)

    • Yoh. 10:22​—Kodi chikondwerero chopereka kachisi kwa Mulungu chinali chiyani? (“chikondwerero cha kupereka kachisi kwa Mulungu” mfundo zimene ndikuphunzira pa Yoh. 10:22, nwtsty)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yoh. 9:1-17

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 14 ¶1-2

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 62

  • Zofunika Pampingo: (15 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 7

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 10 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena