Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 May tsamba 3
  • Muzithandiza Ana Anu Kuti Akhale Otsatira a Khristu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzithandiza Ana Anu Kuti Akhale Otsatira a Khristu
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Makolo, Kodi Mukuthandiza Ana Anu Kuti Ayenerere Kubatizidwa?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Kodi Achinyamata Ayenera Kubatizidwa?
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Zakumapeto
    Gulu Lochita Chifuniro cha Mulungu
  • Ubatizo Ungakuthandizeni Kuti Mukhale Ndi Tsogolo Labwino
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 May tsamba 3
Mnyamata akubatizidwa

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Muzithandiza Ana Anu Kuti Akhale Otsatira a Khristu

Palibe chimene chimawasangalatsa kwambiri makolo achikhristu kuposa kuona kuti mwana wawo ‘akudzikana yekha ndi kunyamula mtengo wake wozunzikirapo n’kumatsatira’ Yesu. (Maliko 8:34; 3 Yoh. 4) Kodi makolo angatani kuti athandize ana awo kuti azitsatira Yesu, adzipereke kwa Yehova komanso kubatizidwa? Kodi ndi zinthu zina ziti zimene zingasonyeze kuti ana anu ndi okonzeka kubatizidwa?

Gulu Lochita Chifuniro cha Yehova

Werengani, “Mawu kwa Makolo Achikhristu” patsamba 165-166 m’buku lakuti Gulu Lochita Chifuniro cha Yehova, kenako yankhani mafunso otsatirawa:

  1. Kodi kukhala wophunzira wa Khristu kumatanthauza chiyani?

  2. Kodi makolo ayenera kuwaphunzitsa chiyani ana awo?

  3. Kodi n’chifukwa chiyani ana ayenera kuyesetsa kutsatira mfundo za m’malemba otsatirawa kuti akhale oyenera kubatizidwa?

    • Akol. 3:20

    • Luka 2:46

    • Sal. 122:1

    • Mat. 4:4

    • Mat. 6:33

    • 1 Akor. 15:33

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena