December 11-17
ZEKARIYA 1-8
Nyimbo Na. 146 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Gwirani Chovala cha Munthu Amene ndi Myuda”: (10 min.)
[Onetsani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Zekariya.]
Zek. 8:20-22—Anthu a mitundu yonse masiku ano akufunafuna Yehova (w14 11/15 27 ¶14)
Zek. 8:23—Anthu amene akuyembekezera kudzakhala padziko lapansili amadzipereka ndi mtima wonse kuthandiza Akhristu odzozedwa (w16.01 23 ¶4; w09 2/15 27 ¶14)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Zek. 5:6-11—Popeza kuipa kuli paliponse m’dzikoli, kodi ifeyo tili ndi udindo wotani? (w17.10 25 ¶18)
Zek. 6:1—Kodi mapiri awiri amkuwa akuimira chiyani? (w17.10 27-28 ¶7-8)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Zek. 8:14-23
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) g17.6 chikuto—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.
Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) g17.6—Sonyezani mmene mungapangire ulendo wobwereza pogwiritsa ntchito magazini imene munamusiyira pa ulendo woyamba. Kenako muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 5 ¶1-2.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
“Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muzilalikira Munthu Aliyense wa M’gawo Lanu”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo yakuti, Kulalikira Mpaka “Kumalekezero a Dziko Lapansi”.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 11 ¶9-21.
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 134 ndi Pemphero