August 28–September 3
EZEKIELI 39-41
Nyimbo Na. 107 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Mmene Masomphenya a Ezekieli Onena za Kachisi Akutikhudzira”: (10 min.)
Ezek. 40:2—Kulambira Yehova n’kokwezeka kwambiri kuposa kulambira kwa mtundu wina uliwonse (w99 3/1 11 ¶16)
Ezek. 40:3, 5—Yehova adzakwaniritsa cholinga chake chokhudza kulambira koyera (w07 8/1 10 ¶2)
Ezek. 40:10, 14, 16—Tiyenera kutsatira mfundo zapamwamba za makhalidwe abwino za Yehova kuti tizimulambira m’njira yovomerezeka (w07 8/1 11 ¶5)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Ezek. 39:7—N’chifukwa chiyani tinganene kuti anthu akamaimba mlandu Mulungu kuti ndi amene amachititsa zinthu zopanda chilungamo, amakhala akudetsa dzina lake? (w12 9/1 21 ¶2)
Ezek. 39:9—Pambuyo pa nkhondo ya Aramagedo, kodi zida zankhondo zimene mitundu idzasiye zidzagwiritsidwa ntchito yotani? (w89 8/15 14 ¶20)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 40:32-47
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) fg phunziro 1 ¶1—Yambani ndi kumufotokozera za vidiyo yakuti Kodi Mungakonde Kumva Uthenga Wabwino? (koma musaonetse vidiyoyi). Kenako perekani kabukuko.
Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) fg phunziro1 ¶2—Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 1 ¶3-4
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
“Kodi Ndingadzachitenso Liti Upainiya Wothandiza?”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo yakuti Yehova Amandithandiza Kuchita Zinthu Zambiri.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 6 ¶1-7 komanso tsamba 58-59
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 92 ndi Pemphero