July 10-16
EZEKIELI 15-17
Nyimbo Na. 11 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Kodi Mumakwaniritsa Zimene Mwalonjeza?”: (10 min.)
Ezek. 17:1-4—Ababulo anachotsa Mfumu Yehoyakini pampando n’kuikapo Zedekiya (w07 7/1 12 ¶6)
Ezek. 17:7, 15—Zedekiya sanakhulupirike, m’malomwake anapempha thandizo kwa Aiguputo (w07 7/1 12 ¶6)
Ezek. 17:18, 19—Yehova ankafuna kuti Zedekiya akwaniritse zomwe analonjeza (w12 10/15 30 ¶11; w88 9/15 17 ¶8)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Ezek. 16:60—Kodi “pangano limene lidzakhalepo mpaka kalekale,” ndi chiyani, ndipo ndi ndani ali m’panganoli? (w88 9/15 17 ¶7)
Ezek. 17:22, 23—Kodi ndi ndani amene ali “nsonga yanthete” yomwe Yehova anati adzabzala? (w07 7/1 12 ¶6)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 16:28-42
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) wp17.4 chikuto—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.
Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) wp17.4 chikuto—Mufotokozereni za vidiyo yakuti N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzira Baibulo? (Koma musaonetse vidiyoyi).
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 11 ¶1-2—Muitanireni kumisonkhano.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Muzikwaniritsa Zimene Munalonjeza pa Tsiku la Ukwati Wanu Ngakhale Pamene Banja Lanu Silikuyenda Bwino: (10 min.) Nkhani yokambidwa ndi mkulu yochokera mu Galamukani! ya March 2014, tsamba 14-15.
Khalani Bwenzi la Yehova—Uzinena Zoona: (5 min.) Onetsani Vidiyo yakuti Khalani Bwenzi la Yehova—Uzinena Zoona. Kenako itanani ana amene munawasankhiratu kuti abwere kutsogolo ndipo afunseni mafunso okhudza vidiyoyi.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 3 ¶13-22, komanso tsamba 36-37, 38
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 137 ndi Pemphero