June 12-18
MALIRO 1-5
Nyimbo Na. 128 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Mtima Wodikira Umatithandiza Kuti Tipirire”: (10 min.)
[Onetsani vidiyo yakuti, Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Maliro.]
Maliro 3:20, 21, 24—Yeremiya anasonyeza kuti anali ndi mtima wodikira ndipo ankadalira Yehova (w12 6/1 14 ¶3-4; w11 9/15 8 ¶8)
Maliro 3:26, 27—Kupirira mayesero kudzatithandiza kuthana ndi mavuto amene tingakumane nawo m’tsogolo (w07 6/1 11 ¶3-4)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Maliro 2:17—Kodi ndi mawu ati kwenikweni amene Yehova “ananena” okhudza Yerusalemu? (w07 6/1 9 ¶2)
Maliro 5:7—Kodi Yehova amaimba anthu mlandu chifukwa cha zolakwa za makolo awo akale? (w07 6/1 10 ¶5)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Maliro 2:20–3:12
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) g17.3 chikuto—Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.
Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) g17.3 chikuto—Muitanireni kumisonkhano yathu.
Nkhani: (Osapitirira 6 min.) w11 9/15 9-10 ¶11-13—Mutu: Yehova Ndi Cholowa Changa.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Zofunika Pampingo: (8 min.) Mukhoza kukambirana “Kalata Yochokera ku Bungwe Lolamulira” ya mu Buku Lapachaka. (yb 17 2-5)
Zimene Gulu Lathu Lachita: (7 min.) Onetsani vidiyo yakuti Zimene Gulu Lathu Lachita ya June 2017.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 2 ¶13-22
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 100 ndi Pemphero