July 11-17
MASALIMO 69-73
Nyimbo Na. 92 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Anthu a Mulungu ndi Odzipereka Potumikira Yehova”: (10 min.)
Sal. 69:9—Tiyenera kumachita zinthu zosonyeza kuti ndife odzipereka kwa Mulungu (w10 12/15 7-11 ndime 2-17)
Sal. 71:17, 18—Akhristu achikulire angathandize achinyamata kukhala odzipereka (w14 1/15 23-25 ndime 4-10)
Sal. 72:3, 12, 14, 16-19—Tikakhala odzipereka timafunitsitsa kuuza ena zimene Ufumu wa Mulungu udzatichitire (w15 10/1 16 ndime 3; w10 8/15 32 ndime 19-20)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Sal. 69:4, 21—Kodi mavesi amenewa akukwaniritsa bwanji ulosi wonena za Mesiya? (w11 8/15 11 ndime 17; w11 8/15 15 ndime 15)
Sal. 73:24—Kodi Yehova amatsogolera bwanji atumiki ake ku ulemerero? (w13 2/15 25-26 ndime 3-4)
Kodi ndaphunzira chiyani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Sal. 73:1-28
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) wp16.4 tsamba loyamba—Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.
Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) wp16.4 tsamba loyamba
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 5 ndime 3 ndi 4
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
“Kodi Mungachite Upainiya kwa Chaka Chimodzi?”: (15 min.) Kambiranani mwachidule nkhaniyi komanso “Ndandanda ya Upainiya Wokhazikika.” Kenako onerani vidiyo ya pa JW Broadcasting ya mutu wakuti, Kusankha Ntchito Imene Sidzatha Mpaka Kalekale. (Pitani pamene alemba kuti MAVIDIYO ENA > ACHINYAMATA.) Mukamaliza kuonera vidiyoyi, kambiranani zimene tikuphunzirapo.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 2 ndime 1-12.
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 123 ndi Pemphero