Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/14 tsamba 4
  • Zilengezo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zilengezo
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 8/14 tsamba 4

Zilengezo

◼ Mabuku ogawira mu August: Tidzagwira ntchito yapadera yogawira kapepala kodziwitsa anthu za webusaiti yathu ya jw.org/ny. September ndi October: Magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! November ndi December: Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? kapena kapepala kakuti, Kodi Mukufuna Kudziwa Choonadi?

◼ Ofesi ya nthambi imasunga mafomu a anthu amene afunsira utumiki wa pa Beteli kwa chaka chimodzi. Ofalitsa obatizidwa amene ali ndi zaka za pakati pa 19 ndi 35 ndipo anatumiza fomu yofunsira utumikiwu, ayenera kutumizanso fomu ina chaka chilichonse ngati sanaitanidwe.

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena