Zilengezo
◼ Mabuku ogawira mu November ndi December: Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? Mungagawirenso timabuku takuti Mverani Mulungu ndi Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha. Mungagwiritsenso ntchito timapepala iti ngati tilipo: Kodi Baibulo Mumalikhulupirira?, Kodi Mukuganiza Kuti Zinthu Zidzakhala Bwanji M’tsogolo?, Kodi N’chiyani Chingathandize Kuti Banja Likhale Losangalala?, Kodi Dziko Lapansili Lili M’manja Mwa Ndani? ndi Kodi Mavuto Amene Tikukumana Nawowa Adzathadi? January ndi February: Gawirani kabuku kakuti, Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu. Ngati mwapeza munthu wachidwi, musonyezeni mmene timapangira phunziro la Baibulo pogwiritsa ntchito timabuku takuti Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu, Mverani Mulungu ndi Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha.