Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/13 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 4/13 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Lemba la Yesaya 24:15 limanena kuti: “M’zilumba zakunyanja adzalemekeza dzina la Yehova.” Mogwirizana ndi mawu amenewa, chaka chatha, pa msonkhano wapadera umene unachitikira pa chilumba cha Chizumulu panasonkhana anthu okwana 50 ndipo anthu awiri anabatizidwa. Pachilumbachi pali mpingo umodzi wokha womwe uli ndi ofalitsa 20 ndipo ulinso ndi apainiya apadera amene akuthandiza kwambiri mpingowu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena