Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/99 tsamba 7
  • Mbiri Yateokalase

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mbiri Yateokalase
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1999
  • Nkhani Yofanana
  • Mbiri Yateokalase
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1999
Utumiki Wathu wa Ufumu—1999
km 5/99 tsamba 7

Mbiri Yateokalase

◼ Albania: Chiŵerengero chapamwamba chatsopano cha ofalitsa 1,556 amene anapereka malipoti m’January chikusonyeza kuti chaposa chiŵerengero cha avareji ya chaka chatha ndi 20 peresenti.

◼ Belau: Chiŵerengero cha December cha ofalitsa 73 chinaposa chiŵerengero cha chaka chatha ndi 20 peresenti ndipo chinaposa chiŵerengero cha m’December wa chaka china cham’buyomo ndi 22 peresenti.

◼ Canada: Pa January 1, 1999, apainiya okhazikika atsopano 460 anaikidwa.

◼ United States: Sosaite inakhazikitsa makomiti osamalira za masoka kuti apereka thandizo kumwera kwa United States kumene zinthu zinawonongeka ndi mikuntho. Izi zinaphatikizapo komwe kunasefukira madzi ku Texas ndi ku Florida Keys komwe mphepo ya Hurricane Georges inawononga zinthu. Oyandikana nawo anadabwa kwambiri ndi njira imene Sosaite inathandizira abale ndi mmene ntchito yopereka thandizoyo inachitikira.

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena