Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w19 February tsamba 32
  • Nkhani Zimene Zatuluka Pa Jw.Org

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zatuluka Pa Jw.Org
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
w19 February tsamba 32

Nkhani Zimene Zatuluka Pa Jw.Org

TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO

Eliya​—Anapirira Mpaka Pamapeto

Eliya anakhalabe wokhulupirika ndipo anakwanitsa kupirira. Chitsanzo chake chingatithandize kulimbitsa chikhulupiriro chathu tikakumana ndi mavuto.

(Pitani pamene alemba kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > KUKHULUPIRIRA MULUNGU.)

BAIBULO LIMASINTHA ANTHU

Sindinkachedwa Kupsa Mtima

Munthu yemwe anali chigawenga amakhulupirira kuti mmene moyo wake ulili panopa ndi umboni wakuti Baibulo lili ndi mphamvu zotha kusintha munthu. Panopa ali pa ubwenzi wolimba ndi Mulungu.

(Pitani pamene alemba kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > MTENDERE KOMANSO MOYO WOSANGALALA.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena