Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
3 Mbiri ya Moyo Wanga—Ndayesetsa Kukhala “Zinthu Zonse kwa Anthu Osiyanasiyana”
MLUNGU WA JANUARY 30, 2017–FEBRUARY 5, 2017
8 Tinamasulidwa ku Uchimo Chifukwa cha Kukoma Mtima Kwakukulu
MLUNGU WA FEBRUARY 6-12, 2017
13 “Kuika Maganizo pa Zinthu za Mzimu Kumabweretsa Moyo ndi Mtendere”
M’buku la Aroma chaputala 6 ndi 8, muli mfundo zothandiza kwambiri Akhristufe. Machaputala amenewa atithandiza kuti tizipindula ndi kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu komanso kuti tiziika maganizo athu pa zinthu zimene zingatibweretsere madalitso amuyaya.
MLUNGU WA FEBRUARY 13-19, 2017
19 Muzimutulira Yehova Nkhawa Zanu Zonse
MLUNGU WA FEBRUARY 20-26, 2017
24 Yehova Amapereka Mphoto kwa Anthu Omufunafuna ndi Mtima Wonse
Nkhani yoyambayi ikufotokoza zimene tingachite kuti titulire Yehova nkhawa zathu. Nkhani yachiwiri ikusonyeza kuti chikhulupiriro chathu chimalimba ngati sitikayikira zoti Yehova amapereka mphoto kwa anthu amene amamufunafuna ndi mtima wonse. Ikusonyezanso kuti madalitso amene Yehova watilonjeza amatithandiza kuti tikhalebe okhulupirika.