Tsamba 32
◼ Kodi ndi ndani amene angakuthandizeni kuti mumvetse bwino Baibulo? Onani masamba 6 mpaka 8.
◼ Kodi n’zotheka kukhala ndi mtendere m’dziko la mavutoli? Onani masamba 10 mpaka 12.
◼ Kodi anthu apezadi chingalawa cha Nowa? Onani masamba 13 ndi 14.
◼ Kodi Abigayeli anali ndani, ndipo ifeyo tingaphunzirepo chiyani pa chikhulupiriro chake? Onani masamba 18 mpaka 21.
◼ Kodi Mulungu amavomereza mitala? Onani tsamba 30.