Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w89 3/1 tsamba 32
  • Chochitika Chofunikira Kukumbukira!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chochitika Chofunikira Kukumbukira!
  • Nsanja ya Olonda—1989
Nsanja ya Olonda—1989
w89 3/1 tsamba 32

Chochitika Chofunikira Kukumbukira!

PANALI pa Nisani 14 ya chaka cha 33 C.E.

Yesu ankagawana chikho cha vinyo ndi mtanda wa mkate wopanda chotupitsa ndi atumwi ake. Malangizo ake? “Chitani ichi chikumbukiro changa.”​—Luka 22:19.

Chotero kamodzi pa chaka, Mboni za Yehova kuzungulira dziko zimakumana pamodzi kukumbukira imfa ya Yesu m’njira imene iye analangizira pa usiku umene iye anapanga ndemanga imeneyo. Chaka chino, Nisani 14 idzayamba pa Lachitatu, March 22, pambuyo pa kuloŵa kwa dzuŵa. Inu mukuitanidwa mothentha kudzagwirizana nafe mu msonkhano wokumbukira umenewu pa madzulo a Lachitatu limenelo. Chonde fufuzani ndi Mboni za Yehova za kumaloko kaamba ka nthaŵi yotsimikizirika ndi malo a kukumanako.

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena