Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g18 No. 2 tsamba 2
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Galamukani!!—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2009
  • Makolo Phunzitsani Ana Anu Mwachikondi
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Chisudzulo Chiridi ndi Minkhole
    Galamukani!—1991
  • Mungatani Kuti Aliyense Azisangalala M’banja Lanu?​—Mbali Yachiwiri
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
Onani Zambiri
Galamukani!!—2018
g18 No. 2 tsamba 2

Mawu Oyamba

Mfundo 12 Zothandiza Kuti Banja Liziyenda Bwino

Nthawi zambiri timamva nkhani zosiyanasiyana zomwe zimasokoneza mabanja. Magaziniyi ikufotokoza zimene anthu ena achita kuti mabanja awo aziyenda bwino.

  • Zaka zapakati pa 1990 ndi 2015, ku United States, chiwerengero cha mabanja omwe anatha chinawirikiza kawiri kwa anthu a zaka zoposa 50 ndipo chinawirikiza katatu kwa anthu a zaka zoposa 65.

  • Makolo ambiri asokonezeka chifukwa akatswiri ena amawauza kuti nthawi zonse aziyamikira ana awo. Pomwe ena amawauza kuti mwana amafunika kumuikira malamulo okhwima.

  • Achinyamata ambiri akukula asanaphunzire luso lililonse lomwe lingadzawathandize m’tsogolo.

Komabe zoona ndi zakuti . . .

  • N’zotheka kukhala ndi banja losangalala komanso kwa moyo wonse.

  • Makolo angakwanitse kulangiza ana awo mwachikondi.

  • Achinyamata akhoza kuphunzira luso linalake lomwe lingadzawathandize akadzakula.

Kodi zimenezi zingatheke bwanji? Werengani Galamukani! iyi kuti mupeze mfundo 12 zothandiza kuti banja liziyenda bwino.

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena