Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g95 8/8 tsamba 32
  • “Sindidzatayanso Makope Ena Ndisanawaŵerenge”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Sindidzatayanso Makope Ena Ndisanawaŵerenge”
  • Galamukani!—1995
Galamukani!—1995
g95 8/8 tsamba 32

“Sindidzatayanso Makope Ena Ndisanawaŵerenge”

Mwamuna wina analembera afalitsi a Galamukani! akumalongosola kuti: “Posachedwapa ndinapeza kope la Galamukani! wa April 8, 1994 pakhomo panga. Iii! Kodi nchiyani chimene chachitika? Mwakonzadi magazini okhala ndi chidziŵitso chamakono a m’ma ‘90.’ Ndinachita chidwi kwambiri ndi mmene nkhani zake zinayambira, ndipo ndinaŵerengadi nkhanizo kwa nthaŵi yoyamba. (Kaŵirikaŵiri ndinkaganiza kuti, ‘Aa, anthu aja anali panonso,’ ndi kutaya magaziniwo.) Mmenemo munali kanthu kena ka aliyense.”

Potsiriza pake iye analemba kuti: “Mwatenga njira yolondola. Pitirizani kuchita ntchito yabwinoyo, ndipo ndikukuuzitsani kuti sindidzatayanso makope ena ndisanawaŵerenge.”

Ngati mungakonde kuti kopa la Galamukani! litumizidwe kunyumba kwanu kapena mufuna kukhala ndi phunziro la Baibulo lapanyumba laulere, chonde lemberani ku Watch Tower, Box 33459, Lusaka 10101, kapena ku keyala yoyenera patsamba 5.

[Mawu a Chithunzi patsamba 32]

Pamwamba: Chilolezo cha ROE/Anglo-Australian Observatory, chithunzi cha David Malin

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena