Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g88 4/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1988
Galamukani!—1988
g88 4/8 tsamba 2

Tsamba 2

Kukongola, kusiyanasiyana, ndi kapangidwe m’chilengedwe kamatsogolera ambiri kukhulupirira kuti payenera kukhala Mlengi wa nzeru. Komabe, kwa ena ambiri, chokhumudwitsa chachikulu cha kukhulupirira kwawo mwa Mulungu kuli kukhalapo kwa kuvutika ndi kuipa m’dziko. Ngati ‘Mulungu ali wachikondi,’ nchifukwa ninji iye amalola zinthu zoipa zambiri chotero kuchitika kwa anthu abwino? Kodi pali zifukwa zenizeni kwa Mulungu za kulolera kuipa? Kodi pali chifukwa chirichonse cha kukhulupirira kuti zoipa zidzatha mtsogolo moyandikira?

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena